Project Hope     home >>stonecroft>> atsogoleri amatsogolera>> phunziro 2>>phunziro 3
Kodi Mulungu ndi wotani? - Phunziro #3
Women's Empowerment Program
Sports Bible Club
Living Water Bible Club

Kodi Mulungu ali kuti?

Purpose of the Lesson
• Begin to understand more about where God is and what He is like
• Recognize God’s nearness and His continual presence
• Recognize His willingness to answer when we call

Pemphero
Mulungu wa mphamvu zonse, ndikufuna ndiphunzire zambiri za Inu.
Ndithandizireni kumvetsetsa ndikudziwa zambiri za Inu pamene
ndikuwerenga mawu anu tsiku ndi tsiku. Ndidziwe kopezeka kwanu
ndikayitanira pa Inu. Ndapemphera mudzina la Yesu Khristu. Amen

Guide’s Comments
This lesson will stretch our minds, as we learn more about who God is and whatHe is like.

His greatness is beyond our imagination. The human mind cannot even begin tocomprehend the awesomeness of God! Our God created everything that has being or existence.

The mysteries and exquisite detail involved in everything God created, even the minute detail in one human cell, is beyond our understanding. How can any human being even begin to understand the God who created all that magnificent detail? He is truly a majestic, all-knowing God.

But, mystery of mysteries, God tells us that He wants us to know Him! Therefore, we know it is possible to know about God because He reveals Himself through the pages of the Bible. The more we read and study the entire Bible and apply its truths to our daily living, the better we will know Him, and the more meaningful our fellowship with Him will be.

Each of the verses in our Weekly Bible Reading gave an answer to our question—where is God? We will take turns giving our answers to each question.

Kuwerenga Baibulo sabata ndi sabata

Tsiku liri lonse msabatali werengani mawu a m’baibulo a tsiku liri lonse
ndi kuyankha funso lotsatira

(Use your Bible or Africa Bible Verse Handbook)

Masalimo 34:18
Mulungu amapezeka kuti mukamufuna?
(God is near people who have broken hearts.)

Masalimo 103:19
Mpando wachifumu wa Mulungu uli kuti?
(God’s throne is in heaven.)

Masalimo 145:18
Kodi ndime imeneyi ikutiwuza chiyani za Mulungu?
(God hears us when we call on Him in our need.)

Yesaya 37:16
Ndime imeneyi ikuti Mulungu amakhala kuti?
(God dwells between the cherubim.)

Yesaya 40:22
Kodi ndime imeneyi ikutiwuza chiyani za komwe kuli Mulungu?
(God sits above the circle of the earth, in heaven.)

Yesaya 43:2
Mulungu amakhala ali kuti pamene muli m’mavuto?
(God is with you, protecting you.)

Yeremiya 23:23
Mulungu amati ali kuti nthawi zonse?
(God is near each one of us. He is never far away, we just fail to recognize Him.)

* Sankhani vesi imodzi mwamavei amene mwawerenga kuchokera mu Baibulo msabatayi, imene yakugwirani mtima panthawi ino. Ganizirani tanthauzo la ndime imeneyi kwa inu ndipo kuti mungayigwiritse ntchito bwanji pa moyo wanu?

Which Bible verse was most meaningful to you?. . . . . How did it affect your week? Tell us what happened. . . . .

All the verses we have read so far in this lesson are from the Old Testament. To see what the New Testament says about where God is, look at Question 1

1. Kodi Mulungu amakhala kuti? 1 Timoteo 6:16
(He lives in light that no one can approach)

Ndikovuta kumufikira Mulungu chifukwa cha kuwala kwa chiyero ndi kupanda banga kopambana kwache. Sikophweka kukhala pamaso pake chifukwa tikudziwiratu kuti ndi ife ochimwa. Koma chifukwa kuti Mulungu amadziwa kuti sitingafanane ndi chiyero chake, amadziwulura yekha kwa ife mu njira yakuti timumvetse. Mwachitsanzo maina ake amawulura za chimene Iye ali.
Timaphunzira kusunthira kufupi ndi Mulungu kudzera mu buku lomwe Iye analemba – Baibulo.

(Use your Bible or Africa Bible Verse Handbook)

2. Kodi baibulo limati chiyani za komwe Mulungu sakhalako?
a. Machitidwe 17:24-25
(He does not live in manmade buildings.)

b. 1 Mafumu 8:27
(Heaven and all space—“heaven of heavens”—is not big enough for Him!

The Bible says God is not limited to living in buildings made for Him, or even limited to the “heaven of heavens,” which we would call space. In the light of what the Bible says, we must say that God does not “live” in the way we think of dwelling in a place.

God’s presence fills all the earth, all of heaven, and all of space. Since the space He made is unlimited, we know that God is even beyond space! Does that help you see what a great God He is?

God is with us, whether we are aware of it or not! Many times He takes care of our needs or keeps us from danger when we are not even aware of it.

Solomon, the king of Israel, built a magnificent temple to the Lord, but recognized that God could not be contained in a temple. His immensity is not limited to a place. He is present everywhere, but all things are not filled to the same degree.

“He does not dwell on earth as He does in heaven, in animals as He does in man, in the inorganic as He does in the organic creation, in the wicked as He does the [righteous], nor in the Church as He does in Christ.”

3. Ngati Mulungu amakhala malo owala kwambiri ovuta kufikako ndipo sakhala mzinyumba kapena m’matchalichi, kodi ndime ya 1 Yohane 4:12 imati padziko lino lapansi, Mulungu amakhala kuti?
. . . . (He lives in union with us.)

Since the book of First John was written to Christians, the “us” in verse 12 refers to people who believe in Jesus; those who have put their trust in Him.

Christian author A.W. Tozer, in speaking of the omnipresence of God said, “God is everywhere here, He is close to everything, next to everyone.”2

Read Isaiah 57:15. . . . . This verse says that although God is completely unapproachable, He reaches down to lift up those who humble themselves before Him. God is above everyone. God is everywhere. There is no place we can hide from Him. Read Jeremiah 23:24 . . . . . God pene¬trates every aspect of our lives. Every place in all the universe and in all of space is filled with His presence.

While God is the Creator of all nature, He is not only the God of nature, but the God of all history. He controls and directs the affairs of all humanity. He is a real, divine person who gives Himself to those who desire a vital relationship with Him. Through Jesus Christ, God is immediately accessible to anyone who wants to come to Him.

4. Lembani momwe mudamvera mutazindikira kupezeka kwa Mulungu kapenanso kuti Mulungu amachita chinthu china chodalitsa pa moyo wanu. Lembani mwatchutchu kuti mudaatani mutaona izi.

(Encourage each person to share.)

God wants to reveal truth about Himself to each of us. He allows things to come into our lives to get our attention, so we will know that we need a power beyond ourselves to live in this ever-changing, sin-filled world.

Read Romans 1:20. . . . .

God has revealed His invisible attributes, His eternal power, and His divine nature to all people through His creation. So people are without excuse, because the only way creation can be explained is to say that God made it.

God has revealed Himself to us in other ways besides the Bible and creation. He reveals Himself to everyone through their consciences. The Bible says that all people have an innate knowledge of God.

Read about it in Romans 2:15 . . . . .

One of the attributes of God which we mentioned in last week’s lesson was His omnipresence. Omni means “all,” so the word means God is present everywhere. God is not bound by space. God, in the total of His being, without being divided, multiplied, or defused, penetrates and fills the whole universe in all its parts. God is everywhere.

5. Kodi kupezeka ponseponse kwa Mulungu kumathunzitsa mtima wanu motani pamene muli m’mavuto?

. . . . (It should be a comfort to know that God is with you all the time no matter what happens. God knows what has happened and why. He also has the power to change things or make good come out of it.)

God will always be present in real and practical ways in our lives.

6. Mavesi otsatirawa akukutsimikizirani za kupezeka kwa Mulungu. Werengani ndipo muloweze zimene zikugwirizana ndi nyengo zanu kapena kuthandizira wina amene mukumudziwa.

Mulungu alinafe

Eksodo 33:14
Ndipo anati, Nkhope yanga idzamuka nawe, ndipo ndidzakupumuza

Masalimo 16:11
Mudzandidziwitsa njira ya moyo: Pankhope pano pali chimwemwe chokwanira; Mdzanja lanu lamanja muli zokondweretsa zomka muyaya.

Masalimo 21:6
Pakuti mumuyikira madalitso kunthawi zonse; mumkonderetsa ndi chimwemwe Pankhope panu.

Masalimo 31:20
Pobisalira pamaso panu mudzawabisa kwa chiwembu cha munthu; Mudzawabisa iwo mumsasa kuti muwalanditse pa kutetana kwa malilime.

Masalimo 46:1
Mulungu ndiye pothawirapo pathu ndi mphamvu yathu, Thandizo lopezekeratu m’masautso.

Masalimo 89:15
Odala anthu odziwa liwu la lipenga; Ayenda mkuunika kwa nkhope yanu, Yehova.

Masalimo 139:7-12
Ndidzapita kuti kuzembetsa mzimu wanu?
Kapena ndidzathawira kuti kuzembera nkhope yanu?
Ndikakwera kunka kumwamba muli komweko;
Kapena ndikadzayalira ku Gehena tawonani, muli komweko.
Ndikazitengera mapiko am’bandakucha ndikukhala kumalekero anyanja; kudzakhala komweko dzanja lanu lidzanditsogolera.
Niridzandigwira dzanja lanu lamanja ndipo ndikati, koma mdima undiphimbe, ndikuwunika kondizinga kukhale usiku;
Ungankhale mdima sudetsa pamaso panu, koma usiku uwala ngati usana: Mdima ukunga kuunika.

Yohane 14:3
Ndipo ngati ndipita kukakonzera inu malo, ndidzabweranso, ndipo ndidzalandira inu kwa Ine ndekha kuti kumene kuli Ineko, mukakhaleko inunso.

* Ngati imodzi mwamavesi amenewa itha kuthandiza kapena kuthunzitsa mtima wa wina wake amene mukumudziwa, konzani njira yabwino yakuti mugawane kapena kumtumikira.

Encourage everyone to tell the memory verse they chose and their plan to share that verse with others.

God wants to be with His people. God knows all things and He always expresses Himself to us in ways that are best for us. He is trustworthy.

The knowledge that we are never alone calms our fears and brings peace to our troubled hearts.

There is another place where God is which we have only implied up to this point. By His Spirit, He lives in the hearts and lives of those who have invited Him in.

When God created man, He breathed eternal life into him and man became a living being. This made man different from all the rest of His creation. Read Genesis 2:7. . . . .

God’s plan is that people live with Him forever. But God gave Adam and Eve, the first humans, the power of choice. And they chose to disobey Him.

The consequence of disobeying God’s revealed will is death—eternal separation from God. Read Deuteronomy 30:19. . . . .

But Adam and Eve’s failure and disobedience did not change God’s plan. God had already provided a way for disobedience to be forgiven and for the sinner to be clean again. When we believe and accept the way God has prepared, we will live forever in fellowship with Him in the place He is preparing for us.
Read 1 John 2:24-25 . . . . .

This gracious action on God’s part reveals more about what God is like. He loves His creation and in mercy, He has graciously provided the only way our relation¬ship with Him can be restored.

Do you remember a time when you made the decision to ask Jesus Christ to come into your life? Have you yielded your life to Him? It is the most important choice we have to make. It is the difference between eternal life with God or apart from God.

We are going to live forever some place. We alone decide where that will be. Don’t postpone this important decision. God wants us to be with Him forever.

God’s presence in our lives makes it possible for us to live under His direction and carry out His purposes! His holy presence with sinful people demonstrates His love and grace.

You may skip Question 7. Since the prayers are personal, do not ask them to share.

.7. Lembani pemphero lanu lanu kwa Mulungu, lowonetsa kukondwera ndi kupezeka kopotilira kwa Iye pa moyo wanu. Pemphero ili simugawana ndi anzanu panthawi yogawana mawu a m’Baibulo. Lembani pempheroli panopo.

In this lesson, we have learned about God’s continual presence in our individual lives. Next week we will learn that God knows each of us personally and loves us intimately.

Closing Prayer
O God, we are overwhelmed by your majesty! How can we ever know the fullness of who You are? You are hidden in light—which cannot be approached. What You are is beyond our ability to express. The Bible plainly tells us that You want us to know You. As we study this next week, open our eyes to see new truths. We worship You. In Jesus’ name, amen.

 

 
 

 

MULUNGU ALI NGATI CHIYANI?

 
 
Copyright ©  2023 www.UnitedCaribbean.com. All rights reserved. Disclaimer Click to Contact us