Project Hope     home >>stonecroft>> atsogoleri amatsogolera>> phunziro 5 >>phunziro 5
Kodi Mulungu ndi wotani? - Phunziro #5
Women's Empowerment Program
Sports Bible Club
Living Water Bible Club

Oyenera kumdziwa Mulungu Ndani?

Purpose of the Lesson
Understand the necessity of the new birth
• Have an opportunity to receive Jesus Christ as Savior
This lesson gives an opportunity to receive Christ

Pemphero
Atate, ndikufuna kudziwa zambiri za Inu. Ndithandizeni kuti ndimvetse zinthu zimene ndikuwerenga. Mwandizizwitsa pakuti zolengedwa zonse ziri pansi panu koma ngankhale ziri choncho mukufuna kuti ine ndikhalebe bwenzi lanu. Ndapemphera mu dzina la Yesu. Amen.

Guide’s Comments
There is only one more session in this study and we have only begun to learn who God is and what He is like. God is much greater than we can ever imagine. All our lives, we will be learning more and more about the wonders of God.

For a quick review, answer the next questions which cover what we have learned so far.

How do we know there is a living God?. . . . . (discuss)

The Bible says God is, He always has been, and always will be. All of creation tells us that God exists. Our own spirits testify to the fact that a personal, loving, faithful, sovereign God made us and we are accountable to Him.

Where is God?. . . . . (discuss)

God is everywhere. He fills all of Earth, heaven, and space. He is even beyond space because He made it all.
When asked why there is only one God, a child gave this answer, “Because God fills every place. There is no room for another one.”

How do we know that God wants us to know Him? . . . . . (discuss)

God told us about Himself in the book He has written, the Bible. Since the beginning of time, God has been revealing what He is like to people. God has demonstrated His love and mercy to us in many different ways throughout our lives, even though we often fail to recognize that things happen as they do because God is working for us.

We have learned about the nature and attributes of God, but we are aware of the fact that to really know all about God is beyond our understanding.

Mulungu sayembekezera kuti tidziwe zonse za Iye, koma amafunitsitsa aliyense adziwe zoonadi zake izi:

  • Mulungu ndi m’modzi, amapezeka mu Utatu: Mulungu Atate, Mwana, ndi Mzimu Woyera
  • Mulungu Atate ndi Mzimu wa Umulungu.
  • Yesu Khristu anabwera padziko lapansi mu Umulungu wake kudzakhala munthu.
  • Ngati Munthu, anakhala pano pa dziko lapansi ndi moyo wangwiro.
  • Anafera pa mtanda, anayikidwa m’manda ndipo anawuka kwa akufa.
  • Atauka, Anabwelera kumwamba mu thupi lake la ulemelero.
  • Mulungu Mzimu Oyera ndi wosaoneka ndi maso, koma ali nafe limodzi panopo.
    Mulungu amatidziwa. Amatidziwa bwino kuposa aliyense. Wakhala akutidziwa. Funso nkumati – Kodi mumamudziwa Mulungu?

To know a lot about God is not knowing Him. What does Jeremiah 29:13 say is the way to gain a deeper knowledge of God? . . . . . (search with all your heart)If a person’s idea of God is shallow, the person’s life is shallow. If someone's atti¬tude about God is deep, his or her Christian life is deep.

Our lesson asks the question, “Who can know God?” And again, we find the answers in our Bible readings.

Kuwerenga Baibulo m’sabata

(Use your Bible or Africa Bible Verse Handbook)

Tsiku liri lonse m’sabata, werengani malo amene mwapatsidwa m’Baibulo kuti muwerenge ndi kuyankha funso lotsatira:

Yohane 14:21-23
Kodi Mulungu adzadziwululira kwa yani?
(To those who obey Him)

Aroma 5:6-9
Ndi chifukwa chiyani Yesu anatifera pamene tinali ochimwa?
(Because He loves us)

1 Timoteo 2:1-6
Ndi ndani amene Yesu akufuna apulumutsidwe?
(Everyone—all people)

Yakobo 4:7-10
Kodi Mulungu amafuna kuti titani kuti Iye akhale pafupi nafe?
(Submit to God, cleanse, purify, and humble ourselves. Come near to God, then He will come near to us.)

2 Petro 3:9
Ndi chifukwa chiyani Mulungu akuchedwa kuweruza dzikoli?
(Submit to God, cleanse, purify, and humble ourselves. Come near to God, then He will come near to us.)

Ahebri 11:6
Mukafika pamaso pa Mulungu, kodi muyenera kukhala ndi chikhulupiliro chotani?
(That He exists and rewards those who seek Him.)

Mateyu 11:27-30
Kodi Mulungu amayitana ndani kuti afike kwa Iye?
(Anyone who is tired of their life as it is—burdened, confused, or restless.)

* Sankhani ndime imodzi mwa ndime zimene mwawerenga kuchokera mu Baibulo msabatayi, imene yakugwirani mtima panthawi ino. Ganizirani tanthauzo la ndime imeneyi kwa inu ndipo kuti mungayigwiritse ntchito bwanji pa moyo wanu?

How did you apply or put into practice the verse you chose? . . . . . Did it affect week? Tell us what happened. . . . .

(Use your Bible or Africa Bible Verse Handbook)

1. Kodi Baibulo limati Chiyani za m’mene munthu angamdziwire Mulungu?
Masalimo 46:10
(Be quiet and stop struggling. Let God be God.)

Masalimo 145:18-19
(Call on the Lord in your need, but have the right motive. This is a precious promise. God says He will hear you.)

Yesaya 55:3
(Listen to His voice and come to Him.)

Ahebri 10:22
(Draw near to Him. Cleanse your hands and purify your hearts.)

Real knowledge of God comes not only from study and research, but from experi-ence and years of living in harmony with the Spirit of God. But if we do not have Christ in our lives, we cannot understand the things of the Spirit.

2. Yesu anauza ophunzira ake za m’mene angamudziwire Mulungu. Werengani Yohane 14:6-7 Ndipo mufotokoze zimene anawawuza.
(The way to know God is to know Jesus.)

Jesus was telling them that He is the way to know what God is like. He is also the way to come to God. He is the way to heaven. He is the only way that leads to eternal life. We can follow Him and know that He will lead us in the right way.

When Jesus said He is the way, the truth, and the life, He was saying He is the truth about God. If we know Jesus, we know what God is like because Jesus is the exact expression of the invisible God.

God is light. Read 1 John 1:5 . . . . . When we are without God, we are in the dark. Sin holds us in bondage. We are sinners by birth and by choice. We are trying to reach the holy God who made us. We fall short, we cannot make it, and we are spiritually dead (Ephesians 2:1). We need help from a source outside of ourselves if we are to become clean so that we can relate to God, who is perfect.

Mulungu amadziwa kuti ndife ochimwa. Amadziwa kuti sitingadzimasule tokha ku tchimoli. Pa Aroma 3:20-24 Baibulo limatiuza momwe tingamasukire ku tchimo.

Liwu lakuti - khulupilira” silikungotanthauza za kuti Yesu Khristu ndi mwana wa Mulungu, amene anapachichikidwa pantanda chifukwa cha machimo anu.

Mawuwa akutanthauza kuyika mtima wanu wonse ndi kumudalira Yesuyo pakulapa machimo anu.

Kulapa ndi kusintha njira ndi kulondola Yesu Khristu. Izi zikutanthauza kuti simuyenera kuyenda njira yanu. Kulapa kumatanthauza kusiya njira zanu zakale ndi kulondola Mulungu.

What did God say about death and life in Ezekiel 18:32? . . . . .

God wants us to live, not die. He tells us to repent so that we will not die. Instead, we will live eternally with Him!

Many people make the mistake of trying to please God by trying to be good. They try to do enough good things to outweigh the bad.

That is the wrong direction. People can never earn their way to heaven or be good enough to enter on their own. Read Romans 3:23 again . . . . . Now turn to Acts 4:12 . . . . .

We must know that we are unable to work our way to heaven. The only answer is the way God has provided. We must put our complete trust in Jesus, His death, and His resurrection.

Kodi mwalandira mphatso ya Mulungu ya chipulumutso?

Ngati mulibe Yesu m’moyo wanu, lankhulani ndi Mulungu mu pemphero, lapani machimo anu, pemphani akukhulukireni nakupatsani moyo wosatha.
Mulungu akukhululukirani chifukwa chikhululukiro komanso moyo wosatha ndi mphatso zimene Iye akufuna kukupatsani. Mphatso izi sizokuyenerani koma mukungoyenera kukhulupilira ndi kuzilandira.

3. Werengani mavesi otsatirawa. Kodi tipange chiyani kuti tilandire mphatso kuchokera kwa Mulungu?
Yohane 6:29
. . . . (Believe in Christ.)

Yohane 5:24
. . . (Believe what God says and receive the gift of eternal life! When you believe, you receive.)

Have you reached out to receive what God wants to give you? Did you pray asking Jesus to come into your life? Read 1 John 5:10-12 . . . . . Do you have God’s Son living in you?

This would be a good opportunity to utilize the Would You Believe It? booklet if there is anyone in your group who has not received Christ.

4. Yesu anauza munthu kuti ayenera kubadwanso mwatsopano. Werengani Yohane 3:1-8 kuti mumve zimene Yesu ananena zakubadwira m’banja la Mulungu?

Lembani tsiku kapena zaka zanu pamene munamkhulupilira ndi kumulandira Yesu kukhala Mbuye ndi Mphulumutsi wa moyo wanu.

Ask for volunteers to briefly tell about the time they accepted Jesus Christ as their Savior and how it has changed their lives. If no one shares, briefly share your testimony with the group.

5. Pamene munkapemphera, kuti Yesu alowe mumtima mwanu, zambiri zodabwitsa zinachitika. Talembani madalitso amane ndime zotsatilazi zikutiwululira.

a) Yohane 3:36
(Eternal life)

b) Yohane 16:24
(Answered prayer brings happiness.)

c) Aroma 4:7-8
(Forgiveness of sin)

d) Aroma 5:1
(We have been put right with God. We have peace with God.)

e) 2 Akorinto 5:17
(You are a new person with a new beginning.)

f) Aefeso 1:13
(You are given the Holy Spirit to live within you.)

g) Ahebri 13:5
(God will never leave or abandon you.)

When we receive Jesus, God gives us eternal life. Our new life is in His Son, Jesus. We are now God’s children and God is our Father. We have been born into His holy family!

Our Creator has become “our perfect parent—
faithful in love and care,
generous and thoughtful,
interested in all we do,
respecting our individuality,
skillful in training us,
wise in guidance,
always available. . .”

God has chosen us to be His children and has given us all the rights and privi¬leges of those who are rightly related to Him. God has chosen you!
Read, Ephesians 1:3-6 . . . . .

Do we value our position as a child of God?

Have we thanked Him for choosing us?

God is now our Heavenly Father. We show Him that we love Him by obeying Him and striving to please Him in all that we do.

We not only have a new relationship with God as our Father, but we have a new relationship with the rest of the world. Every believer is either our brother or sister and everyone else is an individual God wants in His family. We are to share our faith with them as obedient children of God.

We have established the fact that God is the Creator. He is eternal—He always was and always will be. He has all power. He came to earth as a man and is now in heaven.

God provided a Savior through Jesus Christ. Christ’s death on the cross wiped out the debt held against us and set us free. God did this by making an exchange.

Listen to 2 Corinthians 5:21 to identify the exchange, “[God] made Him who knew no sin to be sin on our behalf, that we might become the righteousness of God in Him.” (NASB)

What was the exchange? . . . . . (Our sinful life for His righteous life.)

Jesus had no sin of His own. But He took our sin and, in exchange, He gave us His righteousness. Now, from God’s point of view, we have the righteousness, good¬ness, and purity of Jesus. We know we do not possess those qualities in our¬selves. But God sees us “in Christ” because of this great exchange!

We are in Christ and when God looks at us, He sees Christ’s righteousness. God gives us the life of Christ when we believe. Read Philippians 3:8-9 . . . . . What a wonderful gift God has given us!

Sometimes prayer is a very private experience, but other times we want to share the blessing with others. If you would like to share your prayer with us, we have time to hear it before we finish our study. . . . .

6. Lembani pemphero lanu kwa Mulungu, kumuthokoza pokudziwani ndi pokuwonetsani njira ya m’mene mungakhalire pa ubwebnzi ndi Iye. Mupepmpheni kuti akhale nsanamila yanu nthawi zonse. Pa nthawi imene mukuphunzira mwa kukambirana, mutha kugawana pemphero lanu ndi anzanu.Lembani pemphero lanu pano.

Closing Prayer
Father in Heaven, we thank You for Your gift of salvation. Thank You for making it possible for us to receive all the blessings You have for Your children. As we study our last lesson, help us learn how to live to please You. We pray in Jesus’ name, amen.

 
 

 

MULUNGU ALI NGATI CHIYANI?

 
 
Copyright ©  2023 www.UnitedCaribbean.com. All rights reserved. Disclaimer Click to Contact us