Project Hope     home >>stonecroft>> atsogoleri amatsogolera>> phunziro 5>>phunziro 6
Kodi Mulungu ndi wotani? - Phunziro #6
Women's Empowerment Program
Sports Bible Club
Living Water Bible Club

Ndingamkondweretse bwanji Mulungu?

Purpose of the Lesson
Review the concepts presented in this study
• Understand the attributes of God which are unique to His deity and those which He shares with us
• Recognize God’s holiness
• Understand how to do God’s will and bring glory to God

Pemphero
Atate, Zikomo chifukwa cha zonse zimene ndaphunzira zokhudza Inu. Ndikudziwa kuti sindingamvetsetse za ukulu wanu, chifukwa zifundo zanu ndizochuluka ndipo munthu sangazimvetse. Mudzina la Yesu Khristu ndapemphera. Amen

Inform your group that the Weekly Bible Reading will be discussed at the end of this session.

Guide’s Comments
An evangelist who has spoken in many countries and has ministered to thousands of people said, “The world is full of individuals desperate to know God.”1

People all over the world want to know God. They may have no use for the church. They may not have respect for Christians, but they want to know God. Not only do people want to know God, but God wants people to know Him.

We have studied enough to know that our finite minds cannot comprehend everything about our infinite God. But Moses, who wrote the first five books of the Bible, tells us in Deuteronomy 29:29 that God has already revealed what we need to know about Himself and about our life on earth and in eternity.

1. Mulungu wadziulula Yekha kwa anthu mu njira zisanu:
Mawu ake,
umboni kuchokera kwa okhulupilira okhulupilika,
Chilengedwe chake,
chikumbumtima
Yesu Khristu mwana wake.

Werengani mavesi otsatirawa ndipo potengera m’ndandanda walembedwa pamwambapa, sankhani njira imene Mulungu wadziululira yekha kwa ife.

(Use your Bible or Africa Bible Verse Handbook)

Aroma1:20
(Creation)

2 Petro 1:20-21
(Scripture)

Yohane 1:18
(Jesus—God’s Son has revealed God to us)

Machitidwe 1:8
(Witness of dedicated believers)

1 Timoteo 1:19
(Conscience)

Ubwino wa Mulungu kwa paderadera

Ubwino wina wa Mulungu ndi wapaderadera mu Umulungu wake. Palibe yemwe angakhale ngati Iye. Mulungu ndi:

Wodziyimira komanso wodzipezeketsa yekha.

Wamphamvu zonse

Wopezeka pali ponse

Wanzeru zakuya

Wa ulamuliro wangwiro komanso wopanda malire

 

One of the questions children often ask is, “Who made God?” Children realize that everything they see had a beginning—somebody made it. So they ask, “Who made God?” It is difficult to grasp the idea of God having no origin.

How would you answer if someone asked you, “Who made God?”. . . . . (Pause briefly for their answers. Then give the following answer)

God never needed to be made. He was always here.

God exists in a different way from the way we do. God is eternal. He never had a beginning and He will never die. He is self-existent, which means His continued existence does not depend on any outside source or condition. He is totally independent of anyone or anything. All things exist because of Him. He is the source of all life and all matter. Read John 5:26 . .

Read Revelation 4:11 . . . . . Notice the last line of that verse . . . . . (by God’s will they were given existence and life)

2. Ubwino wina wa Mulungu ndi wapaderadera palibe wina angakhale nawo koma Iye yekha. Komanso ulipo ubwino wina umene Mulungu ali nawo ndipo amagawirako anthu mwa mlingo.

a. Werengani mavesi zotsatirawa ndipo mutchule ma ubwino amene Mulungu amagawana ndi munthu.

1 Yohane 4:16 . . . . (love)

Masalimo 107:1 . . . . (goodness and mercy)

Masalimo 86:15 . . . (compassion and grace)

2 Petro 3:15 . . . . (patience)

Mateyu 6:14 . . . . (ability to forgive)

Mateyu 11:29 . . . . (gentleness and humility)

Afilipo 4:7. . . . (peace)

b. Potengera ma ubwino amene mwalemba pa funso 2a, perekani zitsanzo za momwe mungawonetsere makhalidwewa pa moyo wanu tsiku ndi tsiku.
Mulungu ndi Oyera

 

Even the best of us will never become like God, but we are to be models of the godly qualities God has given us. He wants Christians to be examples of Himself.

God Is Holy
The next question is about a very important attribute of God that we mentioned very briefly in our second lesson. That attribute is holiness.

3 a. Kodi ndi lamulo liti limene Mulungu watipatsa pa 1 Petro 1:16?
(God is holy. He wants us to be holy.)

b. Chingakoke mtima wanu ndi chiyani kuti muyesetse kuti ubwino umenewu uwonekere pa moyo wanu? Ahebri 12:14.
(We want our lives to draw people to God by the holiness they see in us.)


Think about practical things we can do to allow the attributes of God to be seen in us, so others will see His holiness. As we each suggest things, list them on the blank page at the end of the lesson. The title of the list can be Ways to Grow in Christian Living.

You may start the discussion by saying, “I am going to write—Be more faithful in reading the Bible to learn how God wants us to live.” Encourage each person to suggest something that would help them in their Christian life.

God is perfectly holy, righteous, and pure. We are all sinners and fall short of the perfection of God. No one has ever come up to God’s standard of purity, for He is perfect and spotless.

The only way we can please God is by living lives that are clean and obedient to His will. When we receive Christ into our lives and invite Him to live His life in and through us, He is our holiness.

4. Fotokozani mwachidule m’mene mumaganizira kapena m’mene mumawomera mukamaganizira Mulungu. Yankhani mwatchutchu komanso moona za m’mene mumadziwira Mulunguyo.

Encourage each person to share

How did you answer that similar question in Lesson 2, Question 1?. . . . .

Knowledge of God is not only gained by studying the Bible. The Holy Spirit gives us understanding as we live through the varied experiences of our lives. Only those who have God’s Spirit living in them possess this knowledge.

Doing God’s Will

You may say, I have received Jesus into my life as my Savior and Lord, but how can I know what God wants me to do? How can I tell if a thing is something I want to do, or if it is God telling me to do it? . . . . . (Discuss)

God tells us in His Word what He wants us to do. We can check our behavior and activities by the verses listed in Question 5.

5. Werengani ndime zotsatirazi ndipo ndi mawu ochepa lembani chimene Mulungu akufuna kuti inu muchite.

Yohane 13:34-35 …… (Love one another at all times and people will know you are a disciple of Jesus.)

Yohane 14:15 ……(If we love God, we will obey Him.)

Aroma 12:1…..(Offer yourself to God. Dedicate yourself to Him and desire to please Him.)

Aroma 12:2 ….. (Don’t copy the behavior and custom of this world. Instead, let God show you His way for you to live.)

1 Atesolonika 4:3 …. (Live a holy and pure life.)

1 Atesolonika 5:16-18 …. (Be joyful. Keep praying. Be thankful.)

Musanapange chiganizo, tayambani mwadzifunsa mafunso awa

Kodi ndikapanga ichi, chimkondweretsa Mulungu?
Chithandiza?

Kapena chibwezeretsa m’mbuyo ubale wanga ndi Mulungu?

Kodi chisankhochi chiwonetsera chikondi changa pa Mulungu?

Kodi chidziwitsa ena kuti ineyo ndimamukonda Mulungu?

Kodi ndiri ndi njala yochita chifuniro changa kuposa kuchita chifuniro cha Mulungu?

Masalimo 25:4-5. Kumbukirani kuti njira za Mulungu sinjira zathu. Funitsitsa kupanga zonse zimene Mulungu akukuwululirani ndipo adzakuwonetserani cholinga chake pa inu.

One of the things that pleases God and enriches our lives is to study His Word. We have had an opportunity to practice doing that in this Bible study.

6.Poganizira zimene mwaphunzira, nenani zinthu zitatu kapena zinayi zimene mukufuna mutapanga kuti mumkondweretse Mulungu.

Have everyone give their answers to this question. Suggest that they list the good ideas other people give on the blank page at the end of this lesson.

Glory to God

The more we learn about God from His Word, the more aware we are of His purity, holiness, righteousness, and wisdom. The closer we come to the light, the more clearly we can see our sinfulness.

The more aware we are of the utter lack of anything good in us apart from God, the more Jesus Christ can be seen in us!

But, because of our pride, we do not see ourselves as helpless, powerless, and utterly dependent on God.

The greatest blessing we can receive is to know that we are nothing and that we have nothing that will make us acceptable to God. We are helpless, destitute, and completely dependent on God. He offers us His sufficiency when we have no suf-ficiency of our own.

Kodi Mulungu angatipatse Moyo wake? Moyowu tingawulandire pokhapokha titakhala ndi mtima wodzichepetsa. Pamenepo mtima wa phindu ndi wodzipereka umenewu ungadzetse ulemelero pamaso pa Mulungu.

Ngati akhristu tikuyenera kudzifunsa kuti:

Kodi moyo wanga umawonetsera choonadi cha Mulungu?
Kodi Moyo wanga umawonetsera chikondi cha Mulungu?
Kodi moyo wanga umawonetsera chipiliro cha Mulungu?
Kodi ndimakhululuka ngati Mulungu amakhululukira?
Zinthu zoyenera pa kuyenda mu ulemelero wa Mulungu ndi kudzipereka komanso kumusangalatsa Mulunguyo. Tsiku liri lonse monga akhristu, tikuyenera kuwonekera kuti Mzimu wa Mulungu akugonera mwa ife.

Pamene moyo wathu watsiku ndi tsiku ukufotokoza kuti Mulungu ali ngati chiyani, Mulunguyo amagwitilitsa ntchito pofikira ena ndi kubweretsa ulemelero kwa Iye.

What a wonderful way to think of our Christian lives!

7a. Kodi ndi chifukwa chiyani Mulungu analenga Munthu? Yesaya 43:7 …. (for His glory)

b. Kodi tingadzetse bwanji ulemelero kwa Mulungu? Yohane 15:8 ….. (by bearing much fruit, which means that our attitudes and actions show that we live in union with God and show His presence in our lives.)

That is the purpose of our lives—to bring glory to God. In 1 Peter 4:11 we are told of another way we can bring glory to God. . . . . Whatever we do to serve God, we cannot do in our own strength. Instead, we invite God to do it through us in His way. This brings glory to God. Did you know we can glorify God by enjoying fellowship with Him?

Read Psalm 16:11. . . . .

Don’t wait until you get to heaven to enjoy being in God’s presence and having fellowship with Him. That is a bit of heaven you can enjoy right here on earth.

We bring glory to God when we obey Him.

We have read several verses that tell us how we can bring glory to God. What are some of the things that we can do this week which will glorify God? . . . . .

The Weekly Bible Reading answered the question in the title of our lesson, “How Can I Please God?”

Kuwerenga Baibulo m’sabata

(Use your Bible or Africa Bible Verse Handbook)

Tsiku liri lonse msabatayi, Werengani Baibulo malo amene mwapatsidwa ndipo yankhani funso lotsatirali.

Mariko 12:28-31
Nenani mwachidule malamulo awiri a Mulungu aakulu
(To love God with all your being and love everyone else as much as you love yourself.)

Mateyu 4:10
Kodi tiyenera kupembedza ndi kutumikira yani?
(Only worship and serve God)

Mateyu 12:50
Kodi ndi chiyani chimene chimawonetsera kuti tiri pa ubale weni weni ndi Yesu?
(That we do what He wants us to do; obedience)

Yohane 14:23
Mumawonetsera bwanji kuti mumamukonda Mulungu?
(Obey the teaching of the Bible, God’s teaching.)

Afilipo 1:9-11
Kudzachitika chiyani pamene mukusankha zabwino?
(Your life will be filled with good qualities which Christ will form in you.)

1 Akorinto 10:31
Kodi mungadzetse bwanji ulemelero wa Mulungu?
(Do all you do for God’s glory. Remember the importance of the right attitude.)

1 Mbiri 16:23-29
Kodi vesi 29, ikuti anthu adzipanga chiyani?
(Give God glory, bring an offering and worship Him.)

* Sankhani ndime imodzi mwa ndime zimene mwawerenga kuchokera mu Baibulo msabatayi, imene yakugwirani mtima panthawi ino. Ganizirani tanthauzo la ndime imeneyi kwa inu ndipo kuti mungayigwiritse ntchito bwanji pa moyo wanu?

We have learned much about the perfect character and personality of the Holy God we worship. He not only created us, but has provided the way for us to have an intimate relationship with Him. We can choose to live our lives under His control and at the end of this life spend eternity with Him. What a wonderful God He is!

How are we going to put into practice all we have learned about God in this study? Read Colossians 3:1-10. Follow in your New Testaments or Chichewa Bible Verse Handbook as these verses are read. . . . .

8. Lembani pemphero, kumupempha Mulungu kuti akuthandizeni kugwiritsa ntchito zinthu zimene mwaphunzirazi. Muthokozeni chifukwa cha lonjezano lake lakukhala nanu mpaka muyaya. Mutha kugawana pempheroli ndi anzanu ngati mukufuna. Lembani panopo.

To conclude our study, let's praise God together by reading aloud together the verses below from Masalimo 150.....

 

Haleluya!
Lemekezani Mulungu m’malo ake oyera;
Mulemekezeni mthambo la mphamvu yake.
Mlemekezeni chifukwa cha ntchito zake zolimba;
Mlemekezeni monga mwa ukulu wake wa unyinji!
Zonse zakupuma zilemekeze Yehova.
Haleluya!
—Masalimo 150:1-2, 6

 
 

 

MULUNGU ALI NGATI CHIYANI?

 
 
Copyright ©  2023 www.UnitedCaribbean.com. All rights reserved. Disclaimer Click to Contact us